Mawu Amunsi
e Onaninso lemba la Mateyu 19:4-6, pomwe Yesu anafunsa Afarisi funso limodzimodzi kuti: “Kodi simunaŵelenge?” Ngakhale kuti iwo anali ataŵelenga nkhani ya kulengedwa kwa zinthu, ananyalanyaza zimene nkhaniyo inali kuwaphunzitsa za mmene Mulungu amaonela ukwati.