Mawu Amunsi
b MAWU OFOTOKOZELA CITHUNZI: (Pamwamba) Banja likumvetsela nyuzi. Ndiyeno pambuyo pa msonkhano wa mpingo, iwo akuuzako ena maganizo awo pa tanthauzo la zocitika zimene anaona pa nyuzi. (Pansi) Banja likuonelela ciunikilo ca Bungwe Lolamulila kuti liziyendela kamvedwe katsopano pa maulosi a m’Baibo. Iwo akugaŵila zofalitsa zozikika pa Baibo zokonzedwa na kapolo wokhulupilika.