Mawu Amunsi
a Nkhani ino, itithandize kukulitsa ciyamikilo cathu pa mphatso ya Mulungu ya moyo. Tione zimene tingacite kuti tikhalebe athanzi komanso otetezeka tsoka likagwa, na mmene tingapewele ngozi. Tikambilanenso zimene tiyenela kucita kuti nthawi zonse tizikhala okonzeka kulandila cithandizo ca mankhwala tikadwala mwadzidzidzi.