Mawu Amunsi
a Ubatizo ni sitepe yofunika kwambili kwa wophunzila Baibo aliyense. N’ciyani cingalimbikitse wophunzila Baibo kutenga sitepe imeneyi? Ni cikondi. Koma kukonda ciyani komanso ndani? M’nkhani ino, tikambilane mayankho a mafunso amenewa, na mmene umoyo wathu ungakhalile tikabatizika.