Mawu Amunsi
a Anthu ambili amakopeka na coonadi akaona cikondi ceniceni cimene timaonetsana. Komabe, cifukwa ca kupanda ungwilo, nthawi zina cingakhale covuta kucita mwacikondi na Akhristu anzathu. Tiyeni tione cifukwa cake kuonetsana cikondi n’kofunika kwambili, komanso mmene tingatengele citsanzo ca Yesu tikamaona zophophonya za ena.