Mawu Amunsi
b Katswili wina wa Baibo anati: “M’nthawi za anthu ochulidwa m’Baibo, kuceleza unali udindo wapadela. Ndipo munthu akaitanila ena kunyumba kwake sanali kungofunika kukonza cakudya cokwanila basi. Kuti munthu aonetse kuceleza kweni-kweni, maka-maka pa cikwati, anali kufunika kukonza cakudya ca mwana alilenji.”