LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Tikamapeleka ndemanga pa misonkhano ya mpingo, timalimbikitsana wina na mnzake. Ngakhale n’telo, ena amadodoma kupelekapo ndemanga. Koma ena amasangalala kupelekapo ndemanga, ndipo amafuna kuti azipatsidwa mwayi woyankhapo woculukilapo. Pa mbali ziŵilizi, kodi tingaonetse bwanji kuti timaganizila ena, kotelo kuti tonse tilimbikitsidwe? Nanga tingacite ciyani kuti ndemanga zathu zizilimbikitsa abale na alongo pa cikondi na nchito zabwino? Tikambilane zimenezi m’nkhani ino.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani