Mawu Amunsi
a Anthu ambili masiku ano salikhulupilila lonjezo la m’Baibo la dziko latsopano. Iwo amaona kuti ni maloto cabe. Komabe, ndife otsimikiza kuti malonjezo onse a Yehova adzakwanilitsidwa. Ngakhale n’conco, kuti cikhulupililo cathu cikhalebe camoyo, tiyenela kupitiliza kucilimbitsa. Motani? Nkhani ino ifotokoza.