Mawu Amunsi
a Yehova amatitsimikizila kuti amayankha mapemphelo athu ogwilizana na cifunilo cake. Tikakumana na mavuto, timakhala otsimikiza kuti iye adzatithandiza kuti tikhalebe okhulupilika kwa iye. Tiyeni tikambilane mmene Yehova amayankhila mapemphelo athu.