Mawu Amunsi
a Ukwati ni mphatso imene Yehova anapatsa anthu. Mphatso imeneyi imapeleka mwayi kwa okwatilana kusangalala na cikondi capadela pakati pawo. Koma nthawi zina, cikondico cingazime. Ngati muli pabanja, nkhani ino idzakuthandizani kuti cikondi canu cisazime, komanso kuti mukhale na banja lacimwemwe.