Mawu Amunsi
b KUFOTOKOZELA MAWU ENA: Colinga cauzimu, ni ciliconse cimene timayesetsa kucita kuti ticikwanilitse kotelo kuti ticite zambili potumikila Yehova na kum’kondweletsa. Mwacitsanzo, mungadziikile colinga cokulitsa khalidwe linalake lacikhristu, kapena kuwongolela mbali inayake yokhudza kulambila, monga kuŵelenga Baibo, kucita phunzilo la munthu mwini, kapena ulaliki.