Mawu Amunsi
a Akhristu ayenela kukulitsa mantha oyenela pa Mulungu. Mantha otelo angateteze mitima yathu, na kutithandiza kupewa zaciwelewele komanso zamalisece. M’nkhani ino, tikambilane Miyambo caputala 9, imene imachula za akazi aŵili ophiphilitsa, poonetsa kusiyana pakati pa nzelu komanso kupusa. Mfundo za m’caputalaci zingatipindulile masiku ano mpaka muyaya.