LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Kungocokela m’nthawi ya Adamu na Hava, Satana wakhala akulimbikitsa mfundo yakuti anthu ayenela kusankha okha cabwino kapena coipa. Amafuna kuti tiziyendela mfundo imeneyi ponena za malamulo a Yehova, komanso malangizo a gulu amene timalandila. Nkhani ino itithandiza kupewa mzimu wofala umenewu wa dziko la Satanali. Itithandizanso kukhala otsimikiza mtima kuimabe zolimba ku mbali ya Yehova.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani