Mawu Amunsi
a Yehova na Yesu ni ololela, ndipo iwo amafuna kuti nafenso tikulitse khalidwe limeneli. Tikatelo, cidzakhala cosavuta ifenso kusintha pamene zinthu zasintha pa umoyo wathu, monga tikayamba kudwala kapena zacuma zikavuta. Tikakhala ololela tingalimbikitsenso mtendele na mgwilizano mu mpingo.