Mawu Amunsi
a M’dziko la Satanali, anthu si oleza mtima. Ngakhale n’telo, Baibo imatiuza kuti tivale kuleza mtima. Nkhani ino ifotokoza cifukwa cake khalidweli n’lofunika kwambili, komanso mmene tingalikulitsile.
a M’dziko la Satanali, anthu si oleza mtima. Ngakhale n’telo, Baibo imatiuza kuti tivale kuleza mtima. Nkhani ino ifotokoza cifukwa cake khalidweli n’lofunika kwambili, komanso mmene tingalikulitsile.