Mawu Amunsi
a Inu acicepele, Yehova amadziŵa kuti mumakumana na zokhoma zimene zingapangitse kuti cikhale covuta kukhala naye pa ubwenzi. Kodi mungapange bwanji zisankho zanzelu zimene zidzakondweletsa Atate wanu wakumwamba? Tikambilane zitsanzo za anyamata atatu amene anakhala mafumu a Yuda. Onani zimene mungaphunzile pa zisankho zimene anapanga.