Mawu Amunsi
a Pokhala anthu opanda ungwilo, nthawi zina zimativuta kutsatila malangizo ngakhale kuti amene akupeleka malangizowo ali na udindo wocita zimenezo. Nkhani ino ifotokoza mapindu amene amabwela kwa awo amene amamvela makolo awo, “olamulila akulu-akulu,” komanso abale amene akutsogolela mu mpingo wacikhristu.