Mawu Amunsi
b Kuti mupeze malangizo othandiza a mmene mungakambile na makolo anu pa malamulo amene muona kuti ni ovuta kuwatsatila, onani nkhani yakuti “Kodi Ndingakambirane Bwanji ndi Makolo Anga za Malamulo Amene Anakhazikitsa?” pa jw.org ku chichewa.