Mawu Amunsi
a Nkhani ino idzathandiza amene amadzimvela kuti ni ofooka cifukwa ca mavuto, kapena utumiki umene aona kuti sangaukwanitse. Tidzaphunzila mmene Yehova angatilimbikitsile, komanso zimene tiyenela kucita kuti tilandile thandizo lake.
a Nkhani ino idzathandiza amene amadzimvela kuti ni ofooka cifukwa ca mavuto, kapena utumiki umene aona kuti sangaukwanitse. Tidzaphunzila mmene Yehova angatilimbikitsile, komanso zimene tiyenela kucita kuti tilandile thandizo lake.