Mawu Amunsi
a Cimodzi mwa ziphunzitso zozama za mawu a Mulungu n’cokhudza kacisi wauzimu wa Yehova. Kodi kacisi ameneyu n’ciyani? Nkhani ino ifotokoza mfundo zopezeka m’buku la m’Baibo la Aheberi zofotokoza kacisi ameneyu. Lolani kuti nkhani ino ikulitse ciyamikilo canu cimene muli naco pa mwayi wanu wolambila Yehova.