Mawu Amunsi
b Mawu akuti “Yehova wa makamu” amapezeka maulendo 14 m’buku la Hagai. Ndipo anakumbutsa Ayudawo komanso ife masiku ano kuti Yehova ali na mphamvu zopanda malile, ndipo amalamula makamu a zolengedwa zauzimu.—Sal. 103:20, 21.
b Mawu akuti “Yehova wa makamu” amapezeka maulendo 14 m’buku la Hagai. Ndipo anakumbutsa Ayudawo komanso ife masiku ano kuti Yehova ali na mphamvu zopanda malile, ndipo amalamula makamu a zolengedwa zauzimu.—Sal. 103:20, 21.