LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

e MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: M’bale akupempha bwana ake kuti am’patse nthawi yoti apite ku msonkhano wa cigawo. Kenako, akupempha thandizo komanso citsogozo kwa Mulungu pokonzekela kukambanso na bwana wake. Ndiyeno akuonetsa bwana wake kapepala ka ciitanilo ka msonkhanowo, na kumufotokozela kufunika kwa maphunzilo a Baibo amenewo. Bwana wake wacita cidwi ndipo wasintha maganizo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani