Mawu Amunsi
a Timafuna kuti Mulungu atiyanje komanso kutiona olungama. Poseŵenzetsa zimene Paulo na Yakobo analemba, nkhani ino ifotokoza kuti cikhulupililo cathu komanso nchito zathu n’zofunika kuti tiyanjidwe na Yehova.
a Timafuna kuti Mulungu atiyanje komanso kutiona olungama. Poseŵenzetsa zimene Paulo na Yakobo analemba, nkhani ino ifotokoza kuti cikhulupililo cathu komanso nchito zathu n’zofunika kuti tiyanjidwe na Yehova.