Mawu Amunsi
b MAWU OFOTOKOZELA ZITHUNZI: Paulo analimbikitsa Akhristu aciyuda kuika maganizo awo maka-maka pa cikhulupililo, osati pa “nchito za cilamulo,” monga kusokelela ulusi wopota wa buluu ku covala, kukondwelela Pasika, komanso kusamba m’manja kwa mwambo.