Mawu Amunsi
a M’nkhani ino, tikambilane zimene ciyembekezo cacikhristu cimaphatikizapo, komanso cifukwa cake ndife otsimikiza kuti cidzakwanilitsidwa ndithu. Aroma caputala 5 itithandize kuona kusiyana kwa ciyembekezo cimene tili naco panopa, na cimene tinali naco titangoyamba kuphunzila coonadi.