Mawu Amunsi
a Bungwe lina la ku America loona za umoyo linanena kuti kumwa moŵa mopambanitsa ngakhale kwa nthawi yocepa kumabweletsa mavuto monga kuphana, kudzipha, kugona munthu mwacikakamizo, nkhanza kwa mnzako wa mu ukwati, komanso kupita padela.