Mawu Amunsi
a Inu alongo okondedwa acitsikana ndinu a mtengo wapatali mumpingo. Mungafike pa ucikulile wauzimu mwa kukulitsa makhalidwe aumulungu, kuphunzila maluso ofunikila komanso kukonzekela maudindo a m’tsogolo. Mukatelo, mudzasangalala na mautumiki oculuka m’gulu la Yehova.