Mawu Amunsi
b KUFOTOKOZELA MAWU ENA: Munthu amene wakhala Mkhristu wokhwima amatsogoleledwa na Mawu na Mulungu osati na nzelu za dziko. Iye amatengela citsanzo ca Yesu, komanso kucita khama kuti akhale paubale wolimba na Yehova, ndipo amaonetsanso cikondi codzimana kwa ena.