Mawu Amunsi
c Kuti mudziŵe zambili pa mawu akuti “ciwiya cosalimba,” onani nkhani yakuti “Mtengo wa ‘Cotengela Cocepa Mphamvu’” mu Nsanja ya Mlonda ya May 15, 2006, komanso yakuti “Malangizo Anzelu kwa Okwatilana” mu Nsanja ya Mlonda ya March 1, 2005.