Mawu Amunsi
b Mawu a Mulungu salimbikitsa kusalana. Ndipo amakamba momveka bwino kuti kusalana sikupatsa munthu ufulu wokwatilanso. Komabe, pali mikhalidwe ina yovuta imene yapangitsa Akhristu ena kuganizila zosalana. Onani mfundo ya kumapeto 4 yakuti “Kusalana pa Ukwati” m’buku la Kondwelani na Moyo kwa Muyaya!