Mawu Amunsi
a KUFOTOKOZELA MAWU ENA: Mawu akuti “paradaiso wauzimu” amaimila mtendele komanso mgwilizano umene timasangalala nawo polambila Yehova. M’paradaiso wauzimu ameneyu, timasangalala kukhala paubale wabwino na Yehova komanso na anthu ena.
a KUFOTOKOZELA MAWU ENA: Mawu akuti “paradaiso wauzimu” amaimila mtendele komanso mgwilizano umene timasangalala nawo polambila Yehova. M’paradaiso wauzimu ameneyu, timasangalala kukhala paubale wabwino na Yehova komanso na anthu ena.