Mawu Amunsi
b KUFOTOKOZELA MAWU ENA: M’nkhani ino komanso yotsatila, mawu akuti “cibwenzi” atanthauza nthawi pamene mwamuna na mkazi amafuna kudziŵana bwino kuti aone ngati ni oyenelelana kukamanga banja. Cibwenzi cimayamba pa nthawi imene aŵiliwo agwilizana kutelo, mpaka pamene adzagwilizane kucithetsa, kapena kutomelana kuti akakwatilane.