Mawu Amunsi
a KUFOTOKOZELA MAWU ENA: “Mzimu” wochulidwa pa Mateyo 26:41 ni mphamvu ili mwa ife yotipangitsa kumva kukhudzika mtima kapena kucita zimene tikufuna. “Thupi” liimilako kupanda ungwilo kwathu. Conco tingakhale na colinga cabwino cofuna kucita zoyenela, koma tikapanda kusamala, tingagonje ku mayeselo ocita zosemphana na Baibo.