LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

d Mfumu Asa anacita macimo aakulu. (2 Mbiri 16:​7, 10) Ngakhale n’telo, Baibo imakamba kuti iye anacita zoyenela m’maso mwa Yehova. Ngakhale kuti poyamba iye anakana uphungu, n’kutheka kuti pambuyo pake analapa. Yehova anaona zabwino zambili zimene iye anacita kuposa zoipa. Ndipo cofunika kwambili n’cakuti iye analambila Yehova yekhayo, ndipo anayesetsa mwamphamvu kuthetsa kulambila mafano mu ufumu wake.—1 Maf. 15:​11-13; 2 Mbiri 14:​2-5.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani