Mawu Amunsi
a Nkhaniyi inali yapadela. Masiku ano, Yehova sakakamiza munthu wolakwilidwa kukhalabe mu ukwati na munthu amene wacita cigololo. Ndipo mwacikondi, Yehova anauza Mwana wake kufotokoza kuti, mwamuna kapena mkazi angasankhe kuthetsa ukwatiwo ngati angafune kutelo.—Mat. 5:32; 19:9.