Mawu Amunsi
a M’caputala coyambilila cokha ca buku la Aheberi, Paulo anagwila mawu Malemba a Ciheberi maulendo 7 poonetsa kuti kalambilidwe ka Cikhristu kanali kopambana kuposa ka Ciyuda.—Aheb. 1:5-13.
a M’caputala coyambilila cokha ca buku la Aheberi, Paulo anagwila mawu Malemba a Ciheberi maulendo 7 poonetsa kuti kalambilidwe ka Cikhristu kanali kopambana kuposa ka Ciyuda.—Aheb. 1:5-13.