LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Mabuku a Uthenga Wabwino komanso mabuku ena a m’Baibo amaonetsa maulendo angapo pamene Yesu anaonekela kwa ophunzila ake pambuyo poukitsidwa. Iye anaonekela kwa: Mariya Magadala (Yoh. 20:​11-18); kwa azimayi ena (Mat. 28:​8-10; Luka 24:​8-11); kwa ophunzila aŵili (Luka 24:​13-15); kwa Petulo (Luka 24:34); komanso kwa atumwi koma Thomasi sanalipo. (Yoh. 20:​19-24) Anaonekelanso kwa atumwi ndipo Thomasi analipo (Yoh. 20:26); kwa ophunzila 7 (Yoh. 21:​1, 2); kwa ophunzila oposa 500 (Mat. 28:16; 1 Akor. 15:6); kwa m’bale wake Yakobo (1 Akor. 15:7); kwa atumwi onse (Mac. 1:4); komanso kwa atumwi pomwe anali pafupi na mzinda wa Betaniya. (Luka 24:​50-52) N’kutheka kuti olemba Baibo sanachule maulendo onse amene Yesu anaonekela kwa ophunzila ake pambuyo poukitsidwa.—Yoh. 21:25.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani