Mawu Amunsi
d Kuti mudziŵe zimene mungacite kuti muyenelele kutumikila monga mtumiki wothandiza kapena mkulu, ŵelengani nkhani yakuti “Abale—Kodi Mukuyesetsa Kuti Muyenelele Kukhala Mtumiki Wothandiza?” komanso yakuti “Abale—Kodi Mukuyesetsa Kuti Muyenelele Kukhala Mkulu?” mu Nsanja ya Mlonda ya November 2024.