Mawu Amunsi
a KUFOTOKOZELA MAWU ENA: M’nkhani ino, tikambilane zikaiko zimene tingakhale nazo zakuti kodi Yehova amationadi kukhala ofunika, kapena kodi zisankho zomwe tinapanga kumbuyoku zinalidi zanzelu. Apa sitikunena zikaiko zimene Baibo imakambapo zobwela cifukwa copanda cikhulupililo mwa Yehova komanso pa malonjezo ake ayi.