LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Aisiraeli ambili amene anaona cozizwitsa cimene Yehova anacita pa Nyanja Yofiila sanaloŵemo m’Dziko Lolonjezedwa. (Num. 14:​22, 23) Yehova anakamba kuti anthu onse a zaka 20 kupita m’tsogolo adzafela m’cipululu. (Num. 14:29) Komabe, Yoswa, Kalebe, komanso ena ambili amene anali asanakwanitse zaka 20, kuphatikizapo anthu ambili a fuko la Levi, anapulumuka. Iwo anaona kukwanilitsidwa kwa lonjezo la Yehova pamene anawoloka Mtsinje wa Yorodano n’kuloŵa m’dziko la Kanani.—Deut. 1:​24-40.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani