Mawu Amunsi
c Onani nkhani yakuti “Chifukwa Chimene Timakhulupirira Kuti Kuli Mlengi,” mu Galamukani! ya September 2006, komanso bulosha yakuti Mmene Moyo Unayambira—Mafunso 5 Ofunika Kwambiri. Kuti mupeze zitsanzo zina, tambani mavidiyo akuti Zokhudza Mmene Moyo Unayambira pa jw.org ku Chichewa.