Mawu Amunsi
b Ngati munacitidwapo nkhanza, mungapindule mwa kuwelenga nkhani ku Chichewa yakuti “Mfundo Zothandiza Anthu Omwe Achitiridwa Nkhanza Zosiyanasiyana.” Nkhaniyi ipezeka pa mpambo wa nkhani wakuti “Nkhani Zina” pa jw.org komanso mu JW Library®.