LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

f Baibulo silikamba mwachuchuchu zoyenela kapena zosayenela kucita pa nkhani yakucipinda pakati pa mwamuna ndi mkazi wake. Mwamuna aliyense wokwatila wacikhristu pamodzi ndi mkazi wake, ayenela kupanga zisankho pa nkhani imeneyi zoonetsa kuti amalemekeza Yehova, amafuna kusangalatsana bwino, komanso zimene zidzawasiya ndi cikumbumtima coyela. Koma iwo sayenela kukambilana cisawawa ndi anthu ena mmene amaonetselana cikondi mu ukwati wawo.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani