LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Kusonkhanitsa “zinthu zakumwamba” kumene Paulo anachula pa Aefeso 1:​10, n’kosiyana ndi kusonkhanitsa “osankhidwa” kumene Yesu anachula pa Mateyo 24:31 ndi pa Maliko 13:27. Paulo anali kukamba za nthawi pamene Yehova amasankha amene adzalamulila ndi Yesu mwa kuwadzoza ndi mzimu woyela. Koma Yesu anali kukamba za nthawi pamene otsalila odzozedwa adzatengedwele kumwamba cisautso cacikulu cili mkati.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani