LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Yehova anali kukhululukila macimo a anthu amene analiko ngakhale Khristu asanapeleke dipo. Yehova anali kucita zimenezi cifukwa anali kumudalila Mwana wake kuti adzakhalabe wokhulupilika mpaka imfa. Telo kwa Yehova zinali ngati dipo linali litalipilidwa kale.​—Aroma 3:25.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani