Mawu Amunsi
a Kuti mudziwe zambili pa tanthauzo la kuganiza bwino, onani mpambo wa nkhani ku Chichewa wakuti “Kufotokoza Mavesi a m’Baibulo” pankhani yakuti “Kufotokoza 2 Timoteyo 1:7—‘Mulungu Sanatipatse Mzimu Wamantha,’” pansi pa kamutu kakuti “Kuganiza bwino.” Nkhanizi mungazipeze pa jw.org kapena mu JW Library®.