Mawu Amunsi
d Malinga n’zimene zinafotokozedwa mu Ciunikilo Na. 2 ca Bungwe Lolamulila mu 2024, wocotsedwa akapezeka pa msonkhano wa mpingo, wofalitsa angagwilitse nchito cikumbumtima cake cophunzitsidwa Baibo kusankha kumupatsa moni wacidule ndi kumulandila.