Mawu Amunsi
c Mawu amene anawamasulila kuti “kukonda abale” angatanthauze cikondi cimene anthu a mimba imodzi amaonetsana. Koma Paulo anawagwilitsa nchito potanthauza cikondi cacikulu cimene timaonetsana mu mpingo.
c Mawu amene anawamasulila kuti “kukonda abale” angatanthauze cikondi cimene anthu a mimba imodzi amaonetsana. Koma Paulo anawagwilitsa nchito potanthauza cikondi cacikulu cimene timaonetsana mu mpingo.