LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

a Ngakhale munthu wokhulupilika Yobu anayamba kuganizila dzina lake, kapena kuti mbili yake, mopitilila malile anzake atatu atamuneneza kuti anacita colakwa. Poyamba, pamene iye anataikilidwa ana ake ndi katundu wake wonse, “Yobu sanacimwe kapena kuimba Mulungu mlandu woti wacita zinthu zoipa.” (Yobu 1:22; 2:10) Komabe, pamene anamuimba mlandu wakuti anacita zinazake zoipa, anayamba kulankhula “mosaganiza bwino.” Iye anaika kwambili maganizo ake pa kuteteza dzina lake m’malo moyeletsa dzina la Mulungu, kapena kuti mbili yake.​—Yobu 6:3; 13:​4, 5; 32:2; 34:5.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani