LAIBULALI YA PA INTANETI ya Watchtower
Watchtower
LAIBULALI YA PA INTANETI
Cinyanja
  • BAIBO
  • ZOFALITSA
  • MISONKHANO

Mawu Amunsi

b Malemba a Ezekieli 37:1-14, ndi Chivumbulutso 11:7-12, amanena za zinthu zimene zinacitika mu 1919. Ulosi wa pa Ezekieli 37:1-14, umanena za anthu onse a Mulungu amene anayambanso kulambila koona mu 1919, pambuyo pa zaka zambili za ukapolo. Koma lemba la Chivumbulutso 11:7-12, limanena za kagulu kocepa ka abale odzozedwa amene akhala akutsogolela anthu a Mulungu. Kwa kanthawi, abale amenewa analibe ufulu wocita zinthu zauzimu. Koma mu 1919, anayambilanso kucita zinthu zauzimu.

Mabuku a m’Cinyanja (2000-2025)
Tulukani
Loŵani
  • Cinyanja
  • Gawilani
  • Makonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenela Kutsatila
  • Mfundo Yosunga Cisinsi
  • Kusunga Cinsinsi
  • JW.ORG
  • Loŵani
Gawilani